Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 22:22 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene iwo anamva, anazizwa, namsiya Iye, nachokapo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene iwo anamva, anazizwa, namsiya Iye, nachokapo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Atamva zimenezi, anthuwo adathedwa nzeru, motero adamsiya nachokapo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atamva izi, anadabwa, ndipo anamusiya Iye, nachoka.

Onani mutuwo



Mateyu 22:22
10 Mawu Ofanana  

Taonani, Ine ndikutumizani inu monga nkhosa pakati pa mimbulu; chifukwa chake khalani ochenjera monga njoka, ndi oona mtima monga nkhunda.


Ndipo pamene makamu a anthu anamva, anazizwa ndi chiphunzitso chake.


Ndipo sanalimbike mtima munthu aliyense kumfunsa kanthu kuyambira tsiku lomwelo.


Ndipo pakumva ichi, Yesu anazizwa, nati kwa iwo akumtsata, Indetu ndinena kwa inu, ngakhale mwa Israele, sindinapeze chikhulupiriro chotere.


Ndipo anayesa kumgwira Iye; koma anaopa khamu la anthu, pakuti anazindikira kuti Iye anakamba fanizo ili kuwatsutsa iwo; ndipo anamsiya Iye, nachoka.


Pakuti Ine ndidzakupatsani inu kamwa ndi nzeru, zimene adani anu onse sadzatha kuzikana kapena kuzitsutsa.


Ndipo sanathe kuipambana nzeru ndi Mzimu amene analankhula naye.


Mau anu akhale m'chisomo, okoleretsa, kuti mukadziwe inu mayankhidwe anu a kwa yense akatani.