Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 22:14 - Buku Lopatulika

Pakuti oitanidwa ndiwo ambiri, koma osankhidwa ndiwo owerengeka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti oitanidwa ndiwo ambiri, koma osankhidwa ndiwo owerengeka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Yesu adati, “Inde oitanidwa ngambiri, komatu osankhidwa ngoŵerengeka.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Popeza oyitanidwa ndi ambiri koma osankhidwa ndi ochepa.”

Onani mutuwo



Mateyu 22:14
7 Mawu Ofanana  

Chomwecho omalizira adzakhala oyamba, ndipo oyamba adzakhala omalizira.


Ndipo akadaleka kufupikitsidwa masiku awo, sakadapulumuka munthu aliyense: koma chifukwa cha osankhidwawo masiku awo adzafupikitsidwa.


chifukwa Akhristu onama adzauka, ndi aneneri onama nadzaonetsa zizindikiro zazikulu ndi zozizwa: kotero kuti akanyenge, ngati nkotheka, osankhidwa omwe. Onani ndakuuziranitu pasadafike.


Momwemo abale, onjezani kuchita changu kukhazikitsa maitanidwe ndi masankhulidwe anu; pakuti mukachita izi, simudzakhumudwa nthawi zonse;


Iwo adzachita nkhondo pa Mwanawankhosa, ndipo Mwanawankhosa adzawagonjetsa, chifukwa ali Mbuye wa ambuye, ndi Mfumu ya mafumu; ndipo adzawalakanso iwo akukhala naye, oitanidwa, ndi osankhika ndi okhulupirika.