Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 21:40 - Buku Lopatulika

Tsono atabwera mwini munda, adzachitira olimawo chiyani?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tsono atabwera mwini munda, adzachitira olimawo chiyani?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Kodi mwini munda wamphesa uja akadzafika, adzaŵatani alimi aja?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Tsono akabwera mwini munda wamphesa adzachita nawo chiyani matenantiwo?”

Onani mutuwo



Mateyu 21:40
7 Mawu Ofanana  

Ndipo tsopano, inu okhala mu Yerusalemu, ndi anthu a Yuda, weruzanitu mlandu wa ine ndi munda wanga wampesa.


Ndipo pamene nyengo ya zipatso inayandikira, anatumiza akapolo ake kwa olima mundawo, kukalandira zipatso zake.


Ndipo anamtenga iye, namponya kunja kwa munda, namupha.


Iwo ananena kwa Iye, Adzaononga koipa oipawo, nadzapereka mundawo kwa olima ena, amene adzambwezera iye zipatso pa nyengo zake.


Pamenepo mwini munda adzachita chiyani? Adzafika, nadzaononga olimawo, nadzapereka mundawo kwa ena.


ndipo mutani, kulanga koposa kotani nanga adzayesedwa woyenera iye amene anapondereza Mwana wa Mulungu, nayesa mwazi wa chipangano umene anayeretsedwa nao chinthu wamba, nachitira chipongwe Mzimu wa chisomo;