Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 21:4 - Buku Lopatulika

Ndipo ichi chinatero, kuti chikachitidwe chonenedwa ndi mneneri kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ichi chinatero, kuti chikachitidwe chonenedwa ndi mneneri kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Zimenezi zidaatero kuti zipherezere zimene mneneri adaanena kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Izi zinachitika kukwaniritsa zimene zinayankhulidwa ndi mneneri:

Onani mutuwo



Mateyu 21:4
9 Mawu Ofanana  

Kondwera kwambiri, mwana wamkazi wa Ziyoni; fuula mwana wamkazi wa Yerusalemu; taona, Mfumu yako ikudza kwa iwe; ndiye wolungama, ndi mwini chipulumutso; wofatsa ndi wokwera pabulu, ndi mwana wamphongo wa bulu.


Ndipo zonsezi zinakhala kuti chikachitidwe chonenedwa ndi Ambuye mwa mneneri, ndi kuti,


Ndipo munthu akanena kanthu ndi inu, mudzati, Ambuye asowa iwo, ndipo pomwepo adzawatumiza.


Koma izi zonse zinachitidwa, kuti zolembedwa za aneneri zikwaniridwe. Pomwepo ophunzira onse anamsiya Iye, nathawa.


Ndipo anabwera naye mwana wa bulu kwa Yesu, naika zovala zao pa iye, ndipo Iye anakhala pamenepo.


Ndipo anadza naye kwa Yesu; ndipo anayalika zovala zao pa mwana wa buluyo, nakwezapo Yesu.


M'mawa mwake khamu lalikulu la anthu amene adadza kuchikondwerero, pakumva kuti Yesu alinkudza ku Yerusalemu,


Usaope, mwana wamkazi wa Ziyoni; taona mfumu yako idza wokhala pa mwana wa bulu.