Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 21:18 - Buku Lopatulika

Ndipo mamawa, m'mene Iye analinkunkanso kumzinda, anamva njala.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mamawa, m'mene Iye analinkunkanso kumzinda, anamva njala.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

M'maŵa mwake, m'mamaŵa ndithu, pamene Yesu ankabwerera ku Yerusalemu, adaamva njala.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mmamawa, pamene amabwera ku mzinda, anamva njala.

Onani mutuwo



Mateyu 21:18
6 Mawu Ofanana  

Nyengo imeneyo Yesu anapita tsiku la Sabata pakati pa minda ya tirigu; ndipo ophunzira ake anali ndi njala, nayamba kubudula ngala, nadya.


Ndipo pamene Iye analibe kudya masiku makumi anai usana ndi usiku, pambuyo pake anamva njala.


kukayesedwa ndi mdierekezi masiku makumi anai. Ndipo Iye sanadye kanthu masiku awo; ndipo pamene anatha anamva njala.


Pakuti sitili naye mkulu wa ansembe wosatha kumva chifundo ndi zofooka zathu; koma wayesedwa m'zonse monga momwe ife, koma wopanda uchimo.