Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 20:32 - Buku Lopatulika

Ndipo Yesu anaima, nawaitana, nati, Mufuna kuti ndikuchitireni chiyani?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yesu anaima, nawaitana, nati, Mufuna kuti ndikuchitireni chiyani?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adaima, naŵaitana, nkuŵafunsa kuti, “Kodi mukufuna kuti ndikuchitireni chiyani?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu anayima ndi kuwayitana ndipo anawafunsa kuti, “Mukufuna ndikuchitireni chiyani?”

Onani mutuwo



Mateyu 20:32
6 Mawu Ofanana  

Atero Ambuye Yehova, Ichi chomwe adzandipempha a nyumba ya Israele ndiwachitire ichi, ndidzawachulukitsira anthu ngati nkhosa.


Ndipo Iye anati kwa iye, Ufuna chiyani? Iye ananena, Lamulirani kuti ana anga awiri amenewa adzakhale, wina ku dzanja lanu lamanja, ndi wina kulamanzere, mu ufumu wanu.


Ndipo khamulo linawaletsa, kuti atonthole: koma anakuwitsa, nanena, Ambuye, mutichitire chifundo, Inu Mwana wa Davide.


Ananena kwa Iye, Ambuye, kuti maso athu apenye.


chifukwa chakenso ndinadza wosakana, m'mene munatuma kundiitana. Pamenepo ndifunsa, mwandiitaniranji?


Musadere nkhawa konse; komatu m'zonse ndi pemphero, ndi pembedzero, pamodzi ndi chiyamiko, zopempha zanu zidziwike kwa Mulungu.