Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 2:17 - Buku Lopatulika

Pomwepo chinachitidwa chonenedwa ndi Yeremiya mneneri, kuti,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pomwepo chinachitidwa chonenedwa ndi Yeremiya mneneri, kuti,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo zidachitikadi zimene mneneri Yeremiya adaanena kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamenepo, zimene ananena mneneri Yeremiya zinakwaniritsidwa:

Onani mutuwo



Mateyu 2:17
5 Mawu Ofanana  

Mau a Yeremiya mwana wa Hilikiya, wa ansembe amene anali ku Anatoti m'dziko la Benjamini;


nakhalabe kumeneko kufikira atamwalira Herode; kuti chikachitidwe chonenedwa ndi Ambuye mwa mneneri kuti, Ndinaitana Mwana wanga atuluke mu Ejipito.


Pamenepo Herode, poona kuti anampusitsa Anzeruwo, anapsa mtima ndithu, natumiza ena kukaononga tiana tonse ta mu Betelehemu ndi ta m'midzi yake yonse, takufikira zaka ziwiri ndi tating'ono tonse, monga mwa nthawi imeneyo iye anafunsitsa kwa Anzeruwo.


Mau anamveka mu Rama, maliro ndi kuchema kwambiri; Rakele wolira ana ake, wosafuna kusangalatsidwa, chifukwa palibe iwo.


Pamenepo chinakwaniridwa chonenedwa ndi Yeremiya mneneri, ndi kuti, Ndipo iwo anatenga ndalamazo zasiliva makumi atatu, mtengo wa uja wowerengedwa mtengo wake, amene iwo a ana a Israele anawerenga mtengo wake;