Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 19:30 - Buku Lopatulika

Koma ambiri oyamba adzakhala akuthungo, ndi akuthungo adzakhala oyamba.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ambiri oyamba adzakhala akuthungo, ndi akuthungo adzakhala oyamba.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Komatu ambiri amene ali oyambirira adzakhala otsirizira, ndipo amene ali otsirizira adzakhala oyambirira.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma ambiri amene ali oyambirira adzakhala omalizira, ndipo ambiri amene ndi omalizira adzakhala oyambirira.”

Onani mutuwo



Mateyu 19:30
11 Mawu Ofanana  

Chomwecho omalizira adzakhala oyamba, ndipo oyamba adzakhala omalizira.


Koma ambiri akuyamba adzakhala akuthungo, ndi akuthungo adzakhala oyamba.


Ndipo onani, alipo akuthungo amene adzakhala oyamba, ndipo alipo oyamba adzakhala akuthungo.


Munathamanga bwino; anakuletsani ndani kuti musamvere choonadi?


Chifukwa chake tiope kuti kapena likatsala lonjezano lakulowa mpumulo wake, wina wa inu angaoneke ngati adaliperewera.