Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 18:30 - Buku Lopatulika

Ndipo iye sanafune; koma anamuka, namponya iye m'nyumba yandende, kufikira abwezere ngongole.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iye sanafune; koma anamuka, namponya iye m'nyumba yandende, kufikira abwezere ngongole.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma iye adakana, nakamponyetsa m'ndende kuti mpaka abweze ndithu ngongoleyo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Koma iye anakana. Mʼmalo mwake, anachoka nakamumangitsa kufikira atabweza ngongoleyo.

Onani mutuwo



Mateyu 18:30
5 Mawu Ofanana  

ndipo muziti, Itero mfumu, Khazikani uyu m'kaidi, mumdyetse chakudya cha nsautso, ndi madzi a nsautso, mpaka ndikabwera ndi mtendere.


Wotseka makutu ake polira waumphawi, nayenso adzalira koma osamvedwa.


Pamenepo kapolo mnzakeyu anagwada pansi, nampempha iye, nati, Bakandiyembekeza ine, ndipo ndidzakubwezera.


Chifukwa chake m'mene akapolo anzake anaona zochitidwazo, anagwidwa chisoni chachikulu, nadza, nalongosolera mbuye wao zonse zimene zinachitidwa.