Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 17:16 - Buku Lopatulika

Ndipo ndinadza naye kwa ophunzira anu, koma iwo sanathe kumchiritsa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ndinadza naye kwa ophunzira anu, koma iwo sanathe kumchiritsa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndinabwera naye kwa ophunzira anuŵa, koma alephera kumchiritsa.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ine ndinabwera naye kwa ophunzira anu koma alephera kumuchiritsa.”

Onani mutuwo



Mateyu 17:16
7 Mawu Ofanana  

Ambuye, chitirani mwana wanga chifundo; chifukwa adwala khunyu, kuzunzika koipa: pakuti amagwa kawirikawiri pamoto, ndi kawirikawiri m'madzi.


Ndipo Yesu anayankha nati, Ha, obadwa osakhulupirira ndi amphulupulu, ndidzakhala ndi inu nthawi yanji? Ndidzalekerera inu nthawi yanji? Mudze naye kwa Ine kuno.


Ndipo ndinapempha ophunzira anu kuti autulutse; koma sanathe.


Ndipo pa chikhulupiriro cha m'dzina lake dzina lakelo linalimbikitsa iye amene mumuona, nimumdziwa; ndipo chikhulupiriro chili mwa Iye chinampatsa kuchira konse kumeneku pamaso pa inu nonse.