Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 17:14 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene iwo anadza kukhamu la anthu, kunafika kwa Iye munthu, namgwadira Iye, nati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene iwo anadza kukhamu la anthu, kunafika kwa Iye munthu, namgwadira Iye, nati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene iwo adafikanso kumene kunali khamu la anthu kuja, munthu wina adadzagwadira Yesu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atafika ku gulu la anthu, munthu wina anamuyandikira Yesu ndi kugwada pamaso pake.

Onani mutuwo



Mateyu 17:14
8 Mawu Ofanana  

Pomwepo ophunzira anazindikira kuti analankhula nao za Yohane Mbatizi.


Ndipo anadza kwa Iye wodwala khate, nampempha Iye, namgwadira, ndi kunena ndi Iye, Ngati mufuna mukhoza kundikonza.


Ndipo pamene Iye anatuluka kutsata njira, anamthamangira munthu, namgwadira Iye, namfunsa, Mphunzitsi wabwino, ndidzachita chiyani kuti ndilandire moyo wosatha?


Ndipo kunali pamene tidatsiriza masikuwa, tidachoka ndi kunka ulendo wathu; ndipo iwo onse, akazi ndi ana, anatiperekeza kufikira kutuluka m'mzinda; ndipo pogwadira pa mchenga wa kunyanja, tinapemphera,