Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 17:10 - Buku Lopatulika

Ndipo ophunzira ake anamfunsa, nanena, Ndipo bwanji alembi amanena kuti Eliya ndiye atsogole kudza?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ophunzira ake anamfunsa, nanena, Ndipo bwanji alembi amanena kuti Eliya ndiye atsogole kudza?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ophunzira aja adamufunsa kuti, “Nanga bwanji aphunzitsi a Malamulo amati Eliya adzayenera kuyamba wabwera?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ophunzira anamufunsa Iye kuti, “Nanga nʼchifukwa chiyani aphunzitsi amalamulo amati Eliya ayenera kukhala woyamba kubwera?”

Onani mutuwo



Mateyu 17:10
9 Mawu Ofanana  

Ndipo ngati mufuna kulandira, uyu ndiye Eliya amene amati akudza.


Ndipo iwo anati, Ena ati, Yohane Mbatizi; koma ena, Eliya; ndipo enanso Yeremiya, kapena mmodzi wa aneneri.


Ndipo Iye anayankha, nati, Eliya akudzatu, nadzabwezera zinthu zonse;


Ndipo anamfunsa Iye, nanena, Nanga alembi anena kuti adzayamba kufika Eliya?


Ndipo anamfunsa iye, Nanga bwanji? Ndiwe Eliya kodi? Nanena iye, Sindine iye. Ndiwe Mneneriyo kodi? Nayankha, Iai.


Ndipo anamfunsa iye, nati kwa iye, Koma ubatiza bwanji, ngati suli Khristu, kapena Eliya, kapena Mneneriyo?