Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 16:15 - Buku Lopatulika

Iye ananena kwa iwo, Koma inu mutani kuti Ine ndine yani?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Iye ananena kwa iwo, Koma inu mutani kuti Ine ndine yani?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo Yesu adaŵafunsa kuti, “Nanga inuyo, mumati ndine yani?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye anafunsa kuti, “Nanga inuyo mumati ndine yani?”

Onani mutuwo



Mateyu 16:15
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anayankha nati, Chifukwa kwapatsidwa kwa inu kudziwa zinsinsi za Ufumu wa Kumwamba, koma sikunapatsidwe kwa iwo.


Ndipo iwo anati, Ena ati, Yohane Mbatizi; koma ena, Eliya; ndipo enanso Yeremiya, kapena mmodzi wa aneneri.


Ndipo Simoni Petro anayankha nati, Inu ndinu Khristu, Mwana wa Mulungu wamoyo.


Ndipo Iye anawafunsa, Koma inu munena kuti ndine yani? Petro anayankha nanena naye, Ndinu Khristu.


Ndipo anati kwa iwo, Koma inu munena kuti Ine ndine yani? Ndipo anayankha Petro, nati, Khristu wa Mulungu.