Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 16:10 - Buku Lopatulika

Penanso mikate isanu ndi iwiri ija ya anthu zikwi zinai, ndi madengu angati munawatola?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Penanso mikate isanu ndi iwiri ija ya anthu zikwi zinai, ndi madengu angati munawatola?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Sujanso ndi buledi msanu ndi muŵiri ndidadyetsa anthu zikwi zinai? Nanga mudaadzaza madengu angati a zotsala?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kapena buledi musanu ndi muwiri amene anadya anthu 4,000, nanga ndi madengu angati amene munadzaza?

Onani mutuwo



Mateyu 16:10
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anadya onse, nakhuta; ndipo anatola makombo otsala, nadzala madengu khumi ndi iwiri.