Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 15:21 - Buku Lopatulika

Ndipo Yesu anatulukapo napatukira kumbali za Tiro ndi Sidoni.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yesu anatulukapo napatukira kumbali za Tiro ndi Sidoni.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adachoka kumeneko, napita ku madera a ku Tiro ndi Sidoni.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu atachoka kumalo amenewo anapita kudera la ku Turo ndi ku Sidoni.

Onani mutuwo



Mateyu 15:21
9 Mawu Ofanana  

Zebuloni adzakhala m'mphepete mwa nyanja; ndipo iye adzakhala dooko la ngalawa; ndipo malire ake adakhala pa Sidoni.


izi ndizo ziipitsa munthu, koma kudya osasamba manja sikuipitsa munthu ai.


Ndipo Yehova anawapereka m'dzanja la Israele, ndipo anawakantha, nawapirikitsa mpaka ku Sidoni waukulu, ndi ku Misirefoti-Maimu, ndi ku chigwa cha Mizipa ku m'mawa; nawakantha mpaka sanawasiyire ndi mmodzi yense.


nzika zonse za kumapiri kuyambira Lebanoni, mpaka Misirefoti-Maimu, Asidoni onse; ndidzawainga pamaso pa ana a Israele, koma limeneli uwagawire Aisraele, likhale cholowa chao, monga ndinakulamulira.


Asere sanaingitse nzika za ku Ako, kapena nzika za ku Sidoni, kapena a Alabu, kapena a Akizibu, kapena a Heliba, kapena a Afiki, kapena a Rehobu;