Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 15:20 - Buku Lopatulika

izi ndizo ziipitsa munthu, koma kudya osasamba manja sikuipitsa munthu ai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

izi ndizo ziipitsa munthu, koma kudya osasamba manja sikuipitsa munthu ai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Zimenezi ndizo zimaipitsa munthu. Koma kudya chakudya osasamba m'manja, sikungaipitse munthu.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Izi ndi zimene zimachititsa munthu kukhala woyipa; koma kudya ndi mʼmanja mosasamba sikumuchititsa munthu kukhala woyipa.”

Onani mutuwo



Mateyu 15:20
12 Mawu Ofanana  

Pakuti mumtima muchokera maganizo oipa, zakupha, zachigololo, zachiwerewere, zakuba, za umboni wonama, zamwano;


Ophunzira anu alumphiranji miyambo ya makolo? Pakuti sasamba manja pakudya.


Ndipo Yesu anatulukapo napatukira kumbali za Tiro ndi Sidoni.


ndipo simudzalowa konse momwemo kanthu kalikonse kosapatulidwa kapena iye wakuchita chonyansa ndi bodza; koma iwo okha olembedwa m'buku la moyo la Mwanawankhosa.


Koma amantha, ndi osakhulupirira, ndi onyansa, ndi ambanda, ndi achigololo, ndi olambira mafano, ndi onse a mabodza, cholandira chao chidzakhala m'nyanja yotentha ndi moto ndi sulufure; ndiyo imfa yachiwiri.