Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 15:16 - Buku Lopatulika

Ndipo Iye anati, Kodi inunso mukhala chipulukirire?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Iye anati, Kodi inunso mukhala chipulukirire?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adati, “Kani ngakhale inunso simumvetsa?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu anawafunsa kuti, “Kani ngakhale inunso simumvetsa?

Onani mutuwo



Mateyu 15:16
15 Mawu Ofanana  

Mwamvetsa zonsezi kodi? Iwo anati kwa Iye, Inde.


Ndipo Iye anaitana makamuwo nati kwa iwo, Imvani, nimudziwitse;


Ndipo Petro anayankha nati kwa Iye, Mutifotokozere ife fanizoli.


Simudziwa kodi kuti zonse zakulowa m'kamwa zipita m'mimba, ndipo zitayidwa kuthengo?


Bwanji nanga simudziwa kuti sindinanena kwa inu za mikate? Koma pewani chotupitsa cha Afarisi ndi Asaduki.


Kodi chikhalire simudziwa, ndipo simukumbukira mikate isanu ija ya anthu aja zikwi zisanu, ndi madengu angati munawatola?


pakuti sanazindikire za mikateyo, koma mitima yao inauma.


Ndipo ananena nao, Mutero inunso opanda nzeru kodi? Kodi simuzindikira kuti kanthu kalikonse kochokera kunja kukalowa mwa munthu, sikangathe kumdetsa iye;


Koma iwo sanazindikire mauwo, naopa kumfunsa.


Ndipo sanadziwitse kanthu ka izi; ndi mau awa adawabisikira, ndipo sanazindikire zonenedwazo.


Ndipo anawatsegulira mitima yao, kuti adziwitse malembo;


Koma iwo sanadziwitse mau awa, ndipo anabisidwa kwa iwo, kuti asawadziwe; ndipo anaopa kumfunsa za mau awa.


Pakuti mungakhale mwayenera kukhala aphunzitsi chifukwa cha nyengoyi, muli nako kusowanso kuti wina aphunzitse inu zoyamba za chiyambidwe cha maneno a Mulungu; ndipo mukhala onga ofuna mkaka, osati chakudya chotafuna.