Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 15:15 - Buku Lopatulika

Ndipo Petro anayankha nati kwa Iye, Mutifotokozere ife fanizoli.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Petro anayankha nati kwa Iye, Mutifotokozere ife fanizoli.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo Petro adampempha kuti, “Timasulirenitu fanizoli.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Petro anati, “Timasulireni fanizoli.”

Onani mutuwo



Mateyu 15:15
6 Mawu Ofanana  

Ndipo tsono mverani inu fanizolo la wofesa mbeu uja.


Pomwepo Iye anasiya makamuwo, nalowa m'nyumba; ndimo ophunzira ake anadza kwa Iye, nanena, Mutitanthauzire fanizo lija la namsongole wa m'munda.


Ndipo Iye anati, Kodi inunso mukhala chipulukirire?


ndipo sanalankhule nao wopanda fanizo: koma m'tseri anatanthauzira zonse kwa ophunzira ake.


Ndipo m'mene Iye adalowa m'nyumba kusiyana ndi khamulo, ophunzira ake anamfunsa Iye fanizolo.


Ophunzira ake ananena, Onani, tsopano mulankhula zomveka, ndipo mulibe kunena chiphiphiritso.