Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 14:34 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene iwo anaoloka, anafika kumtunda, ku Genesarete.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene iwo anaoloka, anafika kumtunda, ku Genesarete.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono onse adaoloka nyanja nakafika ku Genesarete.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atawoloka, anafika ku Genesareti.

Onani mutuwo



Mateyu 14:34
4 Mawu Ofanana  

Ndipo m'mene amuna a pamenepo anamzindikira, anatumiza konse kudziko lonse lozungulira, nadza nao kwa Iye onse akukhala ndi nthenda;


Ndipo panali, pakumkanikiza khamu la anthu, kudzamva mau a Mulungu, Iye analikuimirira m'mbali mwa nyanja ya Genesarete;