Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 14:18 - Buku Lopatulika

Ndipo Iye anati, Mudze nazo kuno kwa Ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Iye anati, Mudze nazo kuno kwa Ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adati, “Bwera nazoni kuno.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma Iye anati, “Bweretsani kwa Ine.”

Onani mutuwo



Mateyu 14:18
4 Mawu Ofanana  

Koma iwo ananena kwa Iye, Ife tilibe kanthu pano koma mikate isanu, ndi nsomba ziwiri.


Ndipo Iye analamulira makamu a anthu akhale pansi paudzu; ndipo Iye anatenga mikate isanuyo ndi nsomba ziwirizo, ndipo m'mene anayang'ana kumwamba, anadalitsa, nanyema, napatsa mikateyo kwa ophunzira, ndi ophunzira kwa makamuwo.


Ndipo analamulira anthu a khamulo akhale pansi; natenga mikate isanu ndi iwiriyo, nayamika, nanyema, napatsa ophunzira ake, kuti apereke kwa iwo; ndipo anapereka kwa khamulo.


Nati Yesu, Akhalitseni anthu pansi. Ndipo panali udzu wambiri pamalopo. Pamenepo amunawo anakhala pansi, kuwerenga kwao monga zikwi zisanu.