Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 14:12 - Buku Lopatulika

Ndipo ophunzira ake anadza, natola mtembo, nauika; ndipo anadza nauza Yesu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ophunzira ake anadza, natola mtembo, nauika; ndipo anadza nauza Yesu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pambuyo pake ophunzira a Yohane adabwera nadzatenga mtembo wake nkukauika m'manda. Kenaka adapita kukauza Yesu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ophunzira a Yohane anabwera nadzatenga mtembo wake ndi kukawuyika mʼmanda. Pomwepo iwo anapita kukamuwuza Yesu.

Onani mutuwo



Mateyu 14:12
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anautenga mutu wake m'mbalemo, naupatsa buthulo: ndipo iye anamuka nao kwa amake.


Ndipo Yesu pakumva, anachokera kumeneko m'ngalawa, kunka kumalo achipululu pa yekha; ndipo makamu, pamene anamva, anamtsata Iye mumtunda kuchokera m'midzi.


Ndipo m'mene ophunzira ake anamva, anadza nanyamula mtembo wake nauika m'manda.


Ndipo anamuika Stefano anthu opembedza, namlira maliro aakulu.