Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 13:56 - Buku Lopatulika

Ndipo alongo ake sali ndife onsewa? Ndipo Iyeyo adazitenga zinthu zonsezi kuti?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo alongo ake sali ndife onsewa? Ndipo Iyeyo adazitenga zinthu zonsezi kuti?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kodi suja alongo ake onse ali nafe pompano? Nanga tsono zonsezi adazitenga kuti?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kodi alongo ake onse sali ndi ife? Tsono ndi kuti kumene anazitenga zinthu izi?”

Onani mutuwo



Mateyu 13:56
2 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo anakhumudwa chifukwa cha Iye. Koma Yesu anati kwa iwo, Mneneri sakhala wopanda ulemu koma kudziko la kwao ndiko, ndi kubanja kwake.


Si mmisiri wa mitengo uyu, mwana wa Maria, mbale wao wa Yakobo, ndi Yose, ndi Yudasi, ndi Simoni? Ndipo alongo ake sali nafe pano kodi? Ndipo anakhumudwa ndi Iye.