Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 13:26 - Buku Lopatulika

Koma pamene mmera unakula, nubala chipatso, pomwepo anaonekeranso namsongole.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma pamene mmera unakula, nubala chipatso, pomwepo anaonekeranso namsongole.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono pamene mmera udakula nkuyamba kuchita njere, namsongole uja nayenso adayamba kuwoneka.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene tirigu anamera ndi kutulutsa ngala, namsongole anaonekanso.

Onani mutuwo



Mateyu 13:26
4 Mawu Ofanana  

Ndipo inaphuka, nikhala mpesa wotambalala waufupi msinkhu, nthambi zake zinapindikira momwe, ndi mizu yake pansi pake, nikhala mpesa, nuonetsa nthambi ndi kuphuka mphukira.


koma m'mene anthu analinkugona, mdani wake anadza, nafesa namsongole pakati pa tirigu, nachokapo.


Ndipo anyamata ake a mwini nyumbayo anadza, nati kwa iye, Mbuye, kodi simunafese mbeu zabwino m'munda mwanu? Nanga wachokera kuti namsongoleyo?