Ndipo inaphuka, nikhala mpesa wotambalala waufupi msinkhu, nthambi zake zinapindikira momwe, ndi mizu yake pansi pake, nikhala mpesa, nuonetsa nthambi ndi kuphuka mphukira.
Mateyu 13:26 - Buku Lopatulika Koma pamene mmera unakula, nubala chipatso, pomwepo anaonekeranso namsongole. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Koma pamene mmera unakula, nubala chipatso, pomwepo anaonekeranso namsongole. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Tsono pamene mmera udakula nkuyamba kuchita njere, namsongole uja nayenso adayamba kuwoneka. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Pamene tirigu anamera ndi kutulutsa ngala, namsongole anaonekanso. |
Ndipo inaphuka, nikhala mpesa wotambalala waufupi msinkhu, nthambi zake zinapindikira momwe, ndi mizu yake pansi pake, nikhala mpesa, nuonetsa nthambi ndi kuphuka mphukira.
koma m'mene anthu analinkugona, mdani wake anadza, nafesa namsongole pakati pa tirigu, nachokapo.
Ndipo anyamata ake a mwini nyumbayo anadza, nati kwa iye, Mbuye, kodi simunafese mbeu zabwino m'munda mwanu? Nanga wachokera kuti namsongoleyo?