Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 13:18 - Buku Lopatulika

Ndipo tsono mverani inu fanizolo la wofesa mbeu uja.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo tsono mverani inu fanizolo la wofesa mbeu uja.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Tsono inu mumvetse bwino tanthauzo lake la fanizo la munthu wofesa mbeu lija.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Tamverani tsono zimene fanizo la wofesa litanthauza:

Onani mutuwo



Mateyu 13:18
5 Mawu Ofanana  

Pomwepo Iye anasiya makamuwo, nalowa m'nyumba; ndimo ophunzira ake anadza kwa Iye, nanena, Mutitanthauzire fanizo lija la namsongole wa m'munda.


Ndipo pamene anakhala pa yekha, iwo amene anali pafupi ndi Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo anamfunsa za mafanizo.