Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 12:49 - Buku Lopatulika

Ndipo anatambalitsa dzanja lake pa ophunzira ake, nati, Penyani amai wanga ndi abale anga!

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anatambalitsa dzanja lake pa ophunzira ake, nati, Penyani amai wanga ndi abale anga!

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Atatero, adaloza ophunzira ake nati, “Inetu amai anga ndi abale anga ndi aŵa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo akuloza ophunzira ake, Iye anati, “Awa ndiwo amayi anga ndi abale anga.

Onani mutuwo



Mateyu 12:49
7 Mawu Ofanana  

Koma Iye anayankha, nati kwa iye wonenayo, Amai wanga ndani, ndipo abale anga ndi ayani?


Pakuti aliyense amene adzachita chifuniro cha Atate wanga wa Kumwamba, yemweyo ndiye mbale wanga, ndi mlongo wanga, ndi amai wanga.


Ndipo pitani msanga, muuze ophunzira ake, kuti, Wauka kwa akufa; ndipo onani, akutsogolerani ku Galileya; mudzamuona Iye komweko; onani, ndakuuzani inu.


Ndipo anawaunguzaunguza iwo akumzingawo, nanena, Taonani, amai wanga ndi abale anga.


Koma sindipempherera iwo okha, komanso iwo akukhulupirira Ine chifukwa cha mau ao;