Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 12:23 - Buku Lopatulika

Ndipo makamu onse a anthu anazizwa, nanena, Uyu si mwana wa Davide kodi?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo makamu onse a anthu anazizwa, nanena, Uyu si mwana wa Davide kodi?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu onse adazizwa kwambiri nkumanena kuti, “Kodi ameneyu sangakhale Mwana uja wa Davide?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anthu onse anadabwa ndipo anati, “Kodi uyu ndi kukhala mwana wa Davide?”

Onani mutuwo



Mateyu 12:23
9 Mawu Ofanana  

Ndipo onani, mkazi wa ku Kanani anatuluka m'malire, nafuula, nati, Mundichitire ine chifundo Ambuye, mwana wa Davide; mwana wanga wamkazi wagwidwa koopsa ndi chiwanda.


Ndipo mipingo yakumtsogolera ndi yakumtsatira, inafuula, kuti, Hosana kwa Mwana wa Davide! Wolemekezeka ndiye wakudza m'dzina la Ambuye! Hosana mu Kumwambamwamba!


Ndipo panakhala pamene Yesu anatha mau amenewa, makamu a anthu anazizwa ndi chiphunzitso chake:


Ndipo popita Yesu kuchokera kumeneko, anamtsata Iye anthu awiri akhungu, ofuula ndi kuti, Mutichitire ife chifundo, mwana wa Davide.


Ndipo m'mene chinatulutsidwa chiwandacho, wosalankhulayo analankhula, ndipo makamu a anthu anazizwa, nanena, Kale lonse sichinaoneke chomwecho mwa Israele.


Tiyeni, mukaone munthu, amene anandiuza zinthu zilizonse ndinazichita: ameneyu sali Khristu nanga?