Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 12:21 - Buku Lopatulika

Ndipo akunja adzakhulupirira dzina lake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo akunja adzakhulupirira dzina lake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo anthu akunja adzamdalira.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo akunja adzakhulupirira dzina lake.”

Onani mutuwo



Mateyu 12:21
6 Mawu Ofanana  

Ndipo padzakhala tsiku lomwelo, kuti muzu wa Yese umene uima ngati mbendera ya mitundu ya anthu, amitundu adzafunafuna uwu; ndipo popuma pake padzakhala ulemerero.


Iye sadzalephera kapena kudololoka, kufikira atakhazikitsa chiweruzo m'dziko lapansi; ndipo zisumbu zidzalindira chilamulo chake.


Pomwepo anabwera naye kwa Iye munthu wogwidwa ndi chiwanda, wakhungu ndi wosalankhula; ndipo Iye anamchiritsa, kotero kuti wosalankhulayo analankhula, napenya.


kwa iwo amene Mulungu anafuna kuwazindikiritsa ichi chimene chili chuma cha ulemerero wa chinsinsi pakati pa amitundu, ndiye Khristu mwa inu, chiyembekezo cha ulemerero;