Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 12:16 - Buku Lopatulika

nawalimbitsira mau kuti asamuwulule Iye;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

nawalimbitsira mau kuti asamuwulule Iye;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma adaŵalamula kuti asakamuulule.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

nawachenjeza kuti asamuwulule kuti yani.

Onani mutuwo



Mateyu 12:16
7 Mawu Ofanana  

kuti chikachitidwe chonenedwa ndi Yesaya mneneri uja, kuti,


Ndipo pamene anali kutsika paphiri, Yesu anawalamula iwo kuti, Musakauze munthu choonekacho, kufikira Mwana wa Munthu adadzauka kwa akufa.


Ndipo Yesu ananena naye, Ona, iwe, usauze munthu; koma muka, udzionetse wekha kwa wansembe, nupereke mtulo umene anaulamulira Mose, ukhale mboni kwa iwo.


Ndipo maso ao anaphenyuka. Ndipo Yesu anawauzitsa iwo, nanena, Yang'anirani, asadziwe munthu aliyense.


Ndipo Yesu anachokako pamodzi ndi ophunzira ake nanka kunyanja: ndipo linamtsata khamu lalikulu la a ku Galileya, ndi a ku Yudeya,


Ndipo anawalamulira kuti asauze munthu aliyense; koma monga momwe Iye anawalamulitsa momwenso makamaka analalikira kopambana.