Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 10:31 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake musamaopa; inu mupambana mpheta zambiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake musamaopa; inu mupambana mpheta zambiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Choncho musati muziwopa ai. Ndinu a mtengo woposa atimba ambiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Potero musaope; inu ndinu a mtengo woposa mbalame zambiri.

Onani mutuwo



Mateyu 10:31
5 Mawu Ofanana  

Pakuti munamchepsa pang'ono ndi Mulungu, munamveka iye korona wa ulemerero ndi ulemu.


Yang'anirani mbalame za kumwamba, kuti sizimafesa ai, kapena sizimatema ai, kapena sizimatutira m'nkhokwe; ndipo Atate wanu wa Kumwamba azidyetsa. Nanga inu mulibe kusiyana nazo kuziposa kodi?


Lingirirani makwangwala, kuti samafesai, kapena kutemai; alibe nyumba yosungiramo, kapena nkhokwe; ndipo Mulungu awadyetsa; nanga inu simuziposa mbalame kwambiri!