Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 10:30 - Buku Lopatulika

komatu inu, matsitsi onse a m'mutu mwanu awerengedwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

komatu inu, matsitsi onse a m'mutu mwanu awerengedwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inuyotu ngakhale tsitsi lomwe la kumutu kwanu adaliŵerenga lonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo ngakhale tsitsi la mʼmutu mwanu linawerengedwa kale.

Onani mutuwo



Mateyu 10:30
6 Mawu Ofanana  

Nati iye, Mfumu mukumbukire Yehova Mulungu wanu kuti wolipsa mwazi asaonjeze kuononga, kuti angaononge mwana wanga. Niti iyo, Pali Yehova, palibe tsitsi limodzi la mwana wako lidzagwa pansi.


Ndipo Solomoni anati, Iye akakhala munthu woyenera silidzagwa pansi tsitsi lake limodzi lonse; koma mukapezeka mwa iye choipa, adzafadi.


komatu ngakhale matsitsi onse a pamutu panu awerengedwa. Musaopa, muposa mtengo wake wa mpheta zambiri.


Ndipo silidzaonongeka tsitsi limodzi la pamutu panu.


Momwemo ndikuchenjezani mutenge kanthu kakudya; pakuti kumeneku ndi kwa chipulumutso chanu; pakuti silidzatayika tsitsi la pamutu wa mmodzi wa inu.


Ndipo anthuwo ananena ndi Saulo, kodi Yonatani adzafa, amene anachititsa chipulumutso chachikulu ichi mu Israele? Musatero. Pali Yehova, palibe tsitsi limodzi la pamutu wake lidzagwa pansi, pakuti iye anagwirizana ndi Mulungu lero. Chomwecho anthuwo anapulumutsa Yonatani kuti angafe.