Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 10:24 - Buku Lopatulika

Wophunzira saposa mphunzitsi wake, kapena kapolo saposa mbuye wake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wophunzira saposa mphunzitsi wake, kapena kapolo saposa mbuye wake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Paja wophunzira saposa mphunzitsi wake, ndipo wantchito saposa mbuye wake ai.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Wophunzira saposa mphunzitsi wake ndipo wantchito saposa bwana wake.

Onani mutuwo



Mateyu 10:24
6 Mawu Ofanana  

Uriya nanena ndi Davide, Likasalo, ndi Israele, ndi Yuda, alikukhala m'misasa, ndi mbuye wanga Yowabu, ndi anyamata a mbuye wanga alikugona kuthengo, potero ndikapita ine kodi kunyumba yanga kuti ndidye, ndimwe, ndigone ndi mkazi wanga? Pali inu, pali moyo wanu, sindidzachita chinthuchi.


Kumkwanira wophunzira kuti akhale monga mphunzitsi wake, ndi kapolo monga mbuye. Ngati anamutcha mwini banja Belezebulu, sadzaposa kodi kuwatero apabanja ake?


Wophunzira saposa mphunzitsi wake; koma yense, m'mene atakonzedwa mtima, adzafanana ndi mphunzitsi wake.


Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Kapolo sali wamkulu ndi mbuye wake; kapena mtumwi sali wamkulu ndi womtuma iye.


Kumbukirani mau amene Ine ndinanena kwa inu, Kapolo sali wamkulu ndi mbuye wake. Ngati anandilondalonda Ine, adzakulondalondani inunso; ngati anasunga mau anga, adzasunga anunso.