Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 10:12 - Buku Lopatulika

Ndipo polowa m'nyumba muwalonjere.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo polowa m'nyumba muwalonjere.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Poloŵa m'nyumba, muzikanena kuti, ‘Mtendere ukhale ndi inu’.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene mulowa mʼnyumba mupereke moni.

Onani mutuwo



Mateyu 10:12
10 Mawu Ofanana  

M'linga mwako mukhale mtendere, m'nyumba za mafumu mukhale phindu.


Chifukwa cha abale anga ndi mabwenzi anga, ndidzanena tsopano, Mukhale mtendere mwa inu.


Ndipo iwowa, ngakhale akamva kapena akaleka kumva, (pakuti ndiwo nyumba yopanduka,) koma adzadziwa kuti panali mneneri pakati pao.


Ndipo m'mzinda uliwonse, kapena m'mudzi, mukalowamo, mufunsitse amene ali woyenera momwemo; ndipo bakhalani komweko kufikira mutulukamo.


Ndipo ngati nyumbayo ili yoyenera, mtendere wanu udze pa iyo, koma ngati siili yoyenera, mtendere wanu ubwerere kwa inu.


Mau amene anatumiza kwa ana a Israele, akulalikira Uthenga Wabwino wa mtendere mwa Yesu Khristu (ndiye Ambuye wa onse)


Chifukwa chake tili atumiki m'malo mwa Khristu, monga ngati Mulungu alikudandaulira mwa ife; tiumiriza inu m'malo mwa Khristu, yanjanitsidwani ndi Mulungu.


koma ndiyembekeza kukuona iwe msanga, ndipo tidzalankhula popenyana.


ndipo muzitero kwa wodalayo, Mtendere ukhale pa inu, mtendere ukhalenso pa nyumba yanu, ndi mtendere ukhale pa zonse muli nazo.