Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 1:24 - Buku Lopatulika

Ndipo Yosefe anauka tulo take, nachita monga anamuuza mngelo wa Ambuye, nadzitengera yekha mkazi wake;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yosefe anauka tulo take, nachita monga anamuuza mngelo wa Ambuye, nadzitengera yekha mkazi wake;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Yosefe atadzuka, adachita monga momwe mngelo wa Ambuye uja adaamuuzira. Adamtenga Maria, mkazi wake uja,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yosefe atadzuka, anachita zomwe mngelo wa Ambuye uja anamulamulira. Iye anamutenga Mariya kukhala mkazi wake.

Onani mutuwo



Mateyu 1:24
18 Mawu Ofanana  

Chotero anachita Nowa, monga mwa zonse anamlamulira iye Mulungu, momwemo anachita.


Ndipo anachita Nowa monga mwa zonse anamlamulira iye Yehova.


Anatero Mose; monga mwa zonse Yehova adamuuza, momwemo anachita.


Ndipo anayalika hema pamwamba pa Kachisi, naika chophimba cha chihema pamwamba pake; monga Yehova adamuuza Mose.


Nayatsa nyalizo pamaso pa Yehova; monga Yehova adamuuza Mose.


nafukizapo chofukiza cha fungo lokoma; monga Yehova adamuuza Mose.


pakulowa iwo m'chihema chokomanako, ndi pakuyandikiza guwa la nsembe anasamba; monga Yehova adamuuza Mose.


Onani namwali adzaima, nadzabala mwana wamwamuna, ndipo adzamutcha dzina lake, Imanuele. Ndilo losandulika, Mulungu nafe.


ndipo sanamdziwe iye kufikira atabala mwana wake; namutcha dzina lake Yesu.


Muli abwenzi anga inu, ngati muzichita zimene ndikulamulani inu.


Ndipo taonani, mngelo wa Ambuye anaimirirapo, ndipo kuunika kunawala mokhalamo iye; ndipo anakhoma Petro m'nthiti, namuutsa iye, nanena, Tauka msanga. Ndipo maunyolo anagwa kuchoka m'manja mwake.


Koma mngelo wa Ambuye anatsegula pakhomo pa ndende usiku, nawatulutsa, nati,