Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 92:8 - Buku Lopatulika

Koma Inu, Yehova, muli m'mwamba kunthawi yonse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Inu, Yehova, muli m'mwamba kunthawi yonse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu nokha Chauta, ndinu Wopambanazonse mpaka muyaya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma Inu Yehova, ndinu wokwezedwa kwamuyaya.

Onani mutuwo



Masalimo 92:8
13 Mawu Ofanana  

Koma iwo akupatula kutsata njira zao zokhotakhota, Yehova adzawachotsa pamodzi ndi ochita zopanda pake. Mtendere ukhale pa Israele.


Pakuti adzawamweta msanga monga udzu, ndipo adzafota monga msipu wauwisi.


Adani anga afuna kundimeza tsiku lonse, pakuti ambiri andithira nkhondo modzikuza.


mpaka ndinalowa m'zoyera za Mulungu, ndi kulingalira chitsiriziro chao.


Indedi muwaika poterera, muwagwetsa kuti muwaononge.


Kuti adziwe kuti inu nokha, dzina lanu ndinu Yehova, ndinu Wam'mwambamwamba padziko lonse lapansi.


Yehova Wam'mwamba ndiye wamphamvu, wakuposa mkokomo wa madzi ambiri, ndi mafunde olimba a nyanja.


Tsopano ndidziwa kuti Yehova ali wamkulu ndi milungu yonse, pakuti momwe anadzikuza okha momwemo anawaposa.


Ukaona anthu alikutsendereza aumphawi, ndi kuchotsa chilungamo ndi chiweruzo mwachiwawa pa dera lina la dziko, usazizwepo; pakuti mkulu wopambana asamalira; ndipo alipo akulu ena oposa amenewo.


Koma nyengo imeneyo Herode mfumu anathira manja ena a mu Mpingo kuwachitira zoipa.