Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 90:3 - Buku Lopatulika

Mubweza munthu akhale fumbi; nimuti, Bwererani inu, ana a anthu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mubweza munthu akhale fumbi; nimuti, Bwererani inu, ana a anthu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu mumabwezera anthu ku fumbi, ndipo mumati, “Bwererani inu ana a anthu.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu mumabwezera anthu ku fumbi, mumati, “Bwerera ku fumbi iwe mwana wa munthu.”

Onani mutuwo



Masalimo 90:3
8 Mawu Ofanana  

m'thukuta la nkhope yako udzadya chakudya, kufikira kuti udzabwerera kunthaka: chifukwa kuti m'menemo unatengedwa: chifukwa kuti ndiwe fumbi, ndi kufumbiko udzabwerera.


M'dzanja mwake muli mpweya wa zamoyo zonse, ndi mzimu wa munthu aliyense.


Mukabisa nkhope yanu, ziopsedwa; mukalanda mpweya wao, zikufa, ndipo zibwerera kufumbi kwao.


Mpweya wake uchoka, abwerera kunka kunthaka yake; tsiku lomwelo zotsimikiza mtima zake zitayika.


fumbi ndi kubwera pansi pomwe linali kale, mzimu ndi kubwera kwa Mulungu amene anaupereka.


Ine Yehova ndanena, ndidzachitira ndithu ichi khamu ili lonse loipa lakusonkhana kutsutsana nane; adzatha m'chipululu muno, nadzafamo.