Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 88:3 - Buku Lopatulika

Pakuti mzimu wanga wadzala nao mavuto, ndi moyo wanga wayandikira kumanda.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti mzimu wanga wadzala nao mavuto, ndi moyo wanga wayandikira kumanda.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pakuti mtima wanga ndi wodzaza ndi mavuto, moyo wanga ukuyandikira ku malo a anthu akufa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakuti ndili ndi mavuto ambiri ndipo moyo wanga ukuyandikira ku manda.

Onani mutuwo



Masalimo 88:3
15 Mawu Ofanana  

Inde wasendera kufupi kumanda, ndi moyo wake kwa akuononga.


Mtima wao unyansidwa nacho chakudya chilichonse; ndipo ayandikira zipata za imfa.


Akwera kuthambo, atsikira kozama; mtima wao usungunuka nacho choipacho.


Yehova, imvani chilungamo, mverani mfuu wanga; tcherani khutu ku pemphero langa losatuluka m'milomo ya chinyengo.


Tsiku la nsautso yanga ndinafuna Ambuye. Dzanja langa linatambalika usiku, losaleka; mtima wanga unakana kutonthozedwa.


Iye ananyozedwa ndi kukanidwa ndi anthu; munthu wazisoni, ndi wodziwa zowawa; ndipo ananyozedwa monga munthu wombisira anthu nkhope zao; ndipo ife sitinamlemekeze.