Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 83:17 - Buku Lopatulika

Achite manyazi, naopsedwe kosatha; ndipo asokonezeke, naonongeke.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Achite manyazi, naopsedwe kosatha; ndipo asokonezeke, naonongeke.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Achitedi manyazi ndi mantha mpaka muyaya, ndipo afe imfa yonyozeka.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Achite manyazi ndi mantha nthawi zonse; awonongeke mwa manyazi.

Onani mutuwo



Masalimo 83:17
4 Mawu Ofanana  

Otsutsana nane avale manyazi, nadzikute nacho chisokonezo chao ngati ndi chofunda.


Achite manyazi, nadodome iwo akukondwera chifukwa cha choipa chidandigwera. Avekeke ndi manyazi ndi kupunzika iwo akudzikuza pa ine.


Athe nzeru nachite manyazi iwo akufuna moyo wanga; abwezedwe m'mbuyo nasokonezeke iwo akundipangira chiwembu.