Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 83:16 - Buku Lopatulika

Achititseni manyazi pankhope pao; kuti afune dzina lanu, Yehova.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Achititseni manyazi pankhope pao; kuti afune dzina lanu, Yehova.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu Chauta, muŵachititse manyazi, kuti azifunafuna dzina lanu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Muphimbe nkhope zawo ndi manyazi kuti adzafunefune dzina lanu Yehova.

Onani mutuwo



Masalimo 83:16
7 Mawu Ofanana  

Ndikakhala woipa, tsoka ine; ndikakhala wolungama, sindidzakweza mutu wanga; ndadzazidwa ndi manyazi, koma penyani kuzunzika kwanga.


Zoopsa zimgwera ngati madzi; nkuntho umtenga usiku.


Otsutsana nane avale manyazi, nadzikute nacho chisokonezo chao ngati ndi chofunda.


Ndidzawaveka adani ake ndi manyazi; koma pa iyeyu korona wake adzamveka.


Iwo anayang'ana Iye nasanguluka; ndipo pankhope pao sipadzachita manyazi.


Adzachita manyazi, nadzanthunthumira kwakukulu adani anga onse; adzabwerera, nadzachita manyazi modzidzimuka.