Masalimo 80:5 - Buku Lopatulika Munawadyetsa mkate wa misozi, ndipo munawamwetsa misozi yambiri. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Munawadyetsa mkate wa misozi, ndipo munawamwetsa misozi yambiri. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Mwaŵadyetsa chisoni ngati chakudya, mwaŵapatsa misozi ngati chakumwa. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwawadyetsa buledi wa misozi; mwachitisa iwo kumwa misozi yodzaza mbale. |
Misozi yanga yakhala ngati chakudya changa, usana ndi usiku; pakunena iwo kwa ine dzuwa lonse, Mulungu wako ali kuti?
Ndipo ngakhale Ambuye adzakupatsani inu chakudya cha nsautso, ndi madzi a chipsinjo, koma aphunzitsi ako sadzabisikanso, koma maso ako adzaona aphunzitsi ako;