Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 80:12 - Buku Lopatulika

Munapasuliranji maphambo ake, kotero kuti onse akupita m'njira atcherako?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Munapasuliranji maphambo ake, kotero kuti onse akupita m'njira atcherako?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nanga chifukwa chiyani mwagumula mpanda wake, kuti opita m'njira azithyola nawo zipatso zake?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chifukwa chiyani mwagwetsa makoma ake kuti onse amene akudutsa athyole mphesa zake?

Onani mutuwo



Masalimo 80:12
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Hiramu mfumu ya ku Tiro anatuma anyamata ake kwa Solomoni, popeza anamva kuti adamdzoza mfumu m'malo mwa atate wake; pakuti Hiramu adakondana ndi Davide masiku onse.


Ndipo tsopano ndidzakuuzani chimene nditi ndichite ndi munda wanga wampesa; ndidzachotsapo tchinga lake, ndipo zidzadyedwa; ndidzagumula linga lake ndipo zidzapondedwa pansi;


Pakuti Yehova abwezeranso ukulu wake wa Yakobo ngati ukulu wake wa Israele; pakuti okhuthula anawakhuthula, naipsa nthambi zake za mpesa.


Iye adzafika nadzaononga olima munda aja, nadzapatsa munda kwa ena. Ndipo pamene iwo anamva, anati, Musatero iai!