Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 80:10 - Buku Lopatulika

Mthunzi wake unaphimba mapiri, ndi nthambi zake zikunga mikungudza ya Mulungu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mthunzi wake unaphimba mapiri, ndi nthambi zake zikunga mikungudza ya Mulungu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mapiri adaphimbidwa ndi mthunzi wake, mikungudza yaikulu yomwe idaphimbidwa ndi nthambi zake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mapiri anaphimbidwa ndi mthunzi wake, mikungudza yamphamvu ndi nthambi zake.

Onani mutuwo



Masalimo 80:10
2 Mawu Ofanana  

Mitengo ya Yehova yadzala ndi madzi; mikungudza ya ku Lebanoni imene anaioka;


Ndipo ndinatuma mavu atsogolere inu, amene anawaingitsa pamaso panu, ndiwo mafumu awiri a Aamori; osati ndi lupanga lako, kapena ndi uta wako ai.