Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 8:7 - Buku Lopatulika

nkhosa ndi ng'ombe, zonsezo, ndi nyama zakuthengo zomwe;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

nkhosa ndi ng'ombe, zonsezo, ndi nyama za kuthengo zomwe;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

nkhosa, ng'ombe ndi nyama zakuthengo,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

nkhosa, mbuzi ndi ngʼombe pamodzi ndi nyama zakuthengo,

Onani mutuwo



Masalimo 8:7
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anati Mulungu, Tipange munthu m'chifanizo chathu, monga mwa chikhalidwe chathu: alamulire pansomba za m'nyanja, ndi pambalame za m'mlengalenga, ndi pang'ombe, ndi padziko lonse lapansi, ndi pazokwawa zonse zakukwawa padziko lapansi.


Mulungu ndipo anadalitsa iwo, ndipo adati kwa iwo, Mubalane, muchuluke, mudzaze dziko lapansi, muligonjetse: mulamulire pansomba za m'nyanja, ndi pambalame za m'mlengalenga, ndi pazamoyo zonse zokwawa padziko lapansi.


Adamu ndipo anazitcha maina zinyama zonse, ndi mbalame za m'mlengalenga ndi zamoyo zonse za m'thengo: koma kwa Adamu sanapezeke womthangatira iye.