Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 78:51 - Buku Lopatulika

Ndipo anapha ana oyamba onse a mu Ejipito, ndiwo oyamba a mphamvu yao m'mahema a Hamu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anapha ana oyamba onse a mu Ejipito, ndiwo oyamba a mphamvu yao m'mahema a Hamu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adapha ana achisamba onse a Aejipito, ana oyamba a mphamvu zao, m'zithando za zidzukulu za Hamu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anakantha ana oyamba kubadwa a Igupto, zipatso zoyamba kucha za mphamvu zawo mʼmatenti a Hamu

Onani mutuwo



Masalimo 78:51
13 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Hamu: Kusi, ndi Ejipito, ndi Puti, ndi Kanani.


Rubeni, ndiwe woyamba wanga, mphamvu yanga ndi chiyambi cha mphamvu yanga; ulemu wopambana, ndi mphamvu yopambana.


Pamenepo Israele analowa mu Ejipito; ndi Yakobo anakhala mlendo m'dziko la Hamu.


Anaika pakati pao zizindikiro zake, ndi zodabwitsa m'dziko la Hamu.


Ndipo Iye anapha achisamba onse m'dziko mwao, choyambira cha mphamvu yao yonse.


zodabwitsa m'dziko la Hamu, zoopsa ku Nyanja Yofiira.


Anapanda oyamba a Ejipito, kuyambira munthu kufikira zoweta.


Iye amene anapandira Aejipito ana ao oyamba; pakuti chifundo chake nchosatha.


Pakuti ndidzapita pakati padziko la Ejipito usiku womwewo, ndi kukantha ana oyamba onse m'dziko la Ejipito, anthu ndi zoweta; ndipo ndidzachita maweruzo pa milungu yonse ya Aejipito; Ine ndine Yehova.


ndipo kunakhala, pamene Farao anadziumitsa kuti tisamuke, Yehova anawapha onse oyamba kubadwa m'dziko la Ejipito, kuyambira oyamba a anthu, kufikira oyamba a zoweta; chifukwa chake ndimphera nsembe Yehova zazimuna zoyamba kubadwa zonse; koma oyamba onse a ana anga ndiwaombola.


Ndi chikhulupiriro anachita Paska, ndi kuwaza kwa mwazi, kuti wakuononga ana oyamba angawakhudze iwo.