Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 78:41 - Buku Lopatulika

Pakuti anabwerera m'mbuyo, nayesa Mulungu, nachepsa Woyerayo wa Israele.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti anabwerera m'mbuyo, nayesa Mulungu, nachepsa Woyerayo wa Israele.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kaŵirikaŵiri ankamuyesa, ankamputa Woyera wa Israele.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kawirikawiri iwo ankamuyesa Mulungu; ankamuputa Woyera wa Israeli.

Onani mutuwo



Masalimo 78:41
11 Mawu Ofanana  

Ndiye yani wamtonza ndi kumchitira mwano? Ndiye yani wamkwezera mau ndi kumgadamira maso ako m'mwamba? Ndiye Woyerayo wa Israele.


Pakuti chikopa chathu chifuma kwa Yehova; ndi mfumu yathu kwa Woyera wa Israele.


Mtundu wochimwa inu, anthu olemedwa ndi mphulupulu, mbeu yakuchita zoipa, ana amene achita moononga, iwo amsiya Yehova, iwo amnyoza Woyera wa Israele, iwo adana naye nabwerera m'mbuyo.


popeza anthu onse awa amene adaona ulemerero wanga, ndi zizindikiro zanga, ndidazichita mu Ejipito ndi m'chipululu, koma anandiyesa Ine kakhumi aka, osamvera mau anga;


Ndipo anati wina ndi mnzake, Tiike mtsogoleri, tibwerere ku Ejipito.


amene makolo athu sanafune kumvera iye, koma anamkankha achoke, nabwerera m'mbuyo mumtima mwao ku Ejipito,


Musamayesa Yehova Mulungu wanu, monga munamyesa mu Masa.