Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 78:34 - Buku Lopatulika

Pamene anawapha ndipo anamfuna Iye; nabwerera, nafunitsitsa Mulungu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamene anawapha ndipo anamfuna Iye; nabwerera, nafunitsitsa Mulungu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene ankapha ena, otsalira ankayamba kumufunafuna. Ankalapa namafunafuna Mulungu ndi mtima wao wonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mulungu atawapha, iwo amamufunafuna Iyeyo; iwo ankatembenukiranso kwa Iye mwachangu.

Onani mutuwo



Masalimo 78:34
10 Mawu Ofanana  

Yehova, iwo adza kwa Inu movutika, iwo anathira pemphero, muja munalikuwalanga.


Phazi lidzaupondereza pansi; ngakhale mapazi a aumphawi, ndi mapondedwe a osowa.


Iwe wokhala mu Lebanoni, womanga chisa chako m'mikungudza, udzachitidwa chisoni chachikulu nanga pamene mapweteko adzadza kwa iwe, monga mkazi alinkudwala!


Ndidzamuka ndi kubwerera kunka kumalo kwanga, mpaka adzavomereza kupalamula kwao, nafunafuna nkhope yanga; m'msauko mwao adzandifunafuna mwachangu.


Ndipo sanafuulire kwa Ine ndi mtima wao, koma alira pakama pao, asonkhanira tirigu ndi vinyo, apikisana ndi Ine.


Ndipo anthu anadza kwa Mose, nati, Tachimwa, popeza tinanena motsutsana ndi Yehova, ndi inu; pempherani kwa Yehova kuti atichotsere njokazi. Ndipo Mose anawapempherera anthu.


Ndipo ana a Israele anafuula kwa Yehova; pakuti anali nao magaleta achitsulo mazana asanu ndi anai; napsinja ana a Israele kolimba zaka makumi awiri.