Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 78:11 - Buku Lopatulika

Ndipo anaiwala zochita Iye, ndi zodabwitsa zake zimene anawaonetsa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anaiwala zochita Iye, ndi zodabwitsa zake zimene anawaonetsa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Iwo adaiŵala zimene Mulungu adachita, ndiponso zozizwitsa zimene Iye adaŵaonetsa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anayiwala zimene Iye anachita, zozizwitsa zimene anawaonetsa.

Onani mutuwo



Masalimo 78:11
5 Mawu Ofanana  

Koma anaiwala ntchito zake msanga; sanalindire uphungu wake:


Ndi kuti chiyembekezo chao chikhale kwa Mulungu, osaiwala zochita Mulungu, koma kusunga malamulo ake ndiko.


Kodi angathe namwali kuiwala zokometsera zake, kapena mkwatibwi zovala zake? Koma anthu anga andiiwala Ine masiku osawerengeka.


Mwaleka Thanthwe limene linakubalani, mwaiwala Mulungu amene anakulengani.