Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 77:4 - Buku Lopatulika

Mundikhalitsa maso; ndigwidwa mtima wosanena kanthu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mundikhalitsa maso; ndigwidwa mtima wosanena kanthu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mumagwira zikope zanga kuti ndisagone tulo. Ndikuvutika kwambiri kotero kuti sindingathe kulankhula.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Munagwira zikope zanga kuti ndisagone ndipo ndinavutika kwambiri kuti ndiyankhule.

Onani mutuwo



Masalimo 77:4
5 Mawu Ofanana  

Usiku uja tulo tidamwazikira mfumu, niti abwere nalo buku la mbiri, naliwerenga pamaso pa mfumu.


Nakhala pansi pamodzi naye panthaka masiku asanu ndi awiri usana ndi usiku, palibe mmodzi ananena naye kanthu, popeza anaona kuti kuwawaku nkwakukulu ndithu.


Pakuti zikadalemera tsopano koposa mchenga wa kunyanja; chifukwa chake mau anga ndasonthokera kunena.


Ndalema nako kuusa moyo kwanga; ndiyandamitsa kama wanga usiku wonse; mphasa yanga ndiolobza ndi misozi yanga.