Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 76:4 - Buku Lopatulika

Inu ndinu wakuunikira, ndi womveka wakuposa mapiri muli achifwamba.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Inu ndinu wakuunikira, ndi womveka wakuposa mapiri muli achifwamba.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu Mulungu, mukuwonetsa ulemerero ndi mphamvu kupambana mapiri a zofunkha.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Wolemekezeka ndinu, wamphamvu kuposa mapiri amene ali ndi nyama zambiri.

Onani mutuwo



Masalimo 76:4
8 Mawu Ofanana  

Lupanga lao lidzalowa m'mtima mwao momwe, ndipo mauta ao adzathyoledwa.


Mkango wakwera kutuluka m'nkhalango mwake, ndipo waononga amitundu ali panjira, watuluka m'mbuto mwake kuti achititse dziko lako bwinja, kuti mizinda yako ipasuke mulibenso wokhalamo.


Ndipo unayendayenda pakati pa mikango, nukhala msona, nuphunzira kugwira nyama, nulusira anthu.


ndipo ndidzakantha uta wako kuuchotsa m'dzanja lako lamanzere, ndi kutayitsa mivi yako kudzanja lako lamanja.