Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 74:6 - Buku Lopatulika

Ndipo tsopano aphwanya zosemeka zake zonse ndi nkhwangwa ndi nyundo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo tsopano aphwanya zosemeka zake zonse ndi nkhwangwa ndi nyundo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pambuyo pake, ndi nsompho ndi nyundo, adakadzula zosemasema zonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka anaphwanya ndi nkhwangwa ndi akasemasema awo zonse zimene tinapachika.

Onani mutuwo



Masalimo 74:6
4 Mawu Ofanana  

Ndipo m'kati mwa nyumba munali mikungudza yosemasema, ngati zikho ndi maluwa oti gadaa; munali mikungudza yokhayokha simunaoneke mwala ai.


Nalemba m'makoma onse akuzinga chipinda mafano olemba ngati akerubi ndi migwalangwa ndi maluwa oti gadaa, m'katimo ndi kumbuyo kwake.


Zitseko ziwiri zomwe zinali za mtengo wa azitona, anasemapo ngati akerubi ndi migwalangwa ndi maluwa oti gadaa, nawakuta ndi golide; inde anakutanso ndi golide akerubi ndi migwalangwayo.


Ndipo analembapo ngati akerubi ndi migwalangwa ndi maluwa oti gadaa, nakuta zolembazo ndi golide wopsapsala.