Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 73:5 - Buku Lopatulika

Savutika monga anthu ena; sasautsika monga anthu ena.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Savutika monga anthu ena; sasautsika monga anthu ena.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Saona mavuto monga anthu ena, sazunzika ngati anzao.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Saona mavuto monga anthu ena; sazunzika ngati anthu ena onse.

Onani mutuwo



Masalimo 73:5
9 Mawu Ofanana  

Zakuti munthu woipa asungika tsiku la tsoka? Natulutsidwa tsiku la mkwiyo?


Ndikangokumbukira ndivutika mtima, ndi thupi langa lichita nyaunyau.


Nyumba zao sizitekeseka ndi mantha, ngakhale ndodo ya Mulungu siiwakhalira.


Tapenyani, oipa ndi awa; ndipo pokhazikika chikhazikikire aonjezerapo pa chuma chao.


Koma poweruzidwa, tilangidwa ndi Ambuye, kuti tingatsutsidwe pamodzi ndi dziko lapansi.


Koma ngati mukhala opanda chilango, chimene onse adalawako, pamenepo muli am'thengo, si ana ai.


Onse amene ndiwakonda, ndiwadzudzula ndi kuwalanga; potero chita changu, nutembenuke mtima.